Marko 12:10 - Buku Lopatulika10 Kodi simunawerenge ngakhale lembo ili, Mwala umene anaukana omanga nyumba, womwewu unayesedwa mutu wa pangodya: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Kodi simunawerenga ngakhale lembo ili, Mwala umene anaukana omanga nyumba, womwewu unayesedwa mutu wa pangodya: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Nanga monga simudaŵerenge Malembo aja akuti, “ ‘Mwala umene amisiri omanga nyumba adaaukana, womwewo wasanduka mwala wapangondya, wofunika koposa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Kodi simunawerenge lemba lakuti: “ ‘Mwala umene amisiri omanga nyumba anawukana wakhala mwala wa pa ngodya. Onani mutuwo |