Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 12:8 - Buku Lopatulika

8 Ndipo anamtenga, namupha iye, namtaya kunja kwa munda.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndipo anamtenga, namupha iye, namtaya kunja kwa munda.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Tsono adamugwiradi, namupha nkumuponya kunja kwa mundawo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Ndipo anamutenga ndi kumupha, ndipo anamuponya kunja kwa munda wamphesa.

Onani mutuwo Koperani




Marko 12:8
6 Mawu Ofanana  

Mverani fanizo lina: Panali munthu, mwini banja, amene analima munda wampesa, nauzunguniza linga, nakumba umo moponderamo mphesa, namanga nsanja, naukongoletsa kwa olima munda, namuka kwina.


Ndipo anamtenga iye, namponya kunja kwa munda, namupha.


Koma olima ajawo, ananena mwa iwo okha, Ameneyu ndiye wolowa nyumba; tiyeni timuphe iye, ndipo mundawu udzakhala wathu.


Pamenepo mwini munda adzachita chiyani? Adzafika, nadzaononga olimawo, nadzapereka mundawo kwa ena.


Ndipo anamponya kunja kwa mundawo, namupha. Pamenepo mwini munda wampesawo adzawachitira chiyani?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa