Marko 12:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo anamtenga, namupha iye, namtaya kunja kwa munda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo anamtenga, namupha iye, namtaya kunja kwa munda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Tsono adamugwiradi, namupha nkumuponya kunja kwa mundawo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Ndipo anamutenga ndi kumupha, ndipo anamuponya kunja kwa munda wamphesa. Onani mutuwo |