Marko 12:7 - Buku Lopatulika7 Koma olima ajawo, ananena mwa iwo okha, Ameneyu ndiye wolowa nyumba; tiyeni timuphe iye, ndipo mundawu udzakhala wathu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Koma olima ajawo, ananena mwa iwo okha, Ameneyu ndiye wolowa nyumba; tiyeni timuphe iye, ndipo mundawu udzakhala wathu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Koma alimi aja adayamba kuuzana kuti, ‘Ameneyu ndiye amene ati adzamsiyire chumachi. Tiyeni timuphe kuti chidzakhale chathu.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 “Koma alimi aja anati kwa wina ndi mnzake, ‘Uyu ndi mlowamʼmalo. Tiyeni timuphe, ndipo cholowacho chidzakhala chathu.’ Onani mutuwo |