Marko 12:6 - Buku Lopatulika6 Anamtsalira mmodzi, ndiye mwana wake wokondedwa; potsiriza anamtuma iye kwa iwo, nanena, Adzamchitira ulemu mwana wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Anamtsalira mmodzi, ndiye mwana wake wokondedwa; potsiriza anamtuma iye kwa iwo, nanena, Adzamchitira ulemu mwana wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 “Munthu uja adangotsala ndi mmodzi basi, mwana wake weniweni wapamtima. Ndiye pambuyo pa onse adadzatuma iyeyu. Adati, ‘Mwana wanga yekhayu akamchitira ulemu.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 “Munthu uja anatsala ndi mwana mmodzi, wamwamuna amene amamukonda. Pomaliza anamutumiza mwanayo nati, ‘Adzamuchitira ulemu mwana wanga.’ Onani mutuwo |