Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 12:4 - Buku Lopatulika

4 Ndipo anatumanso kapolo wina kwa iwo; ndipo ameneyu anamlasa mutu, namchitira zomchititsa manyazi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ndipo anatumanso kapolo wina kwa iwo; ndipo ameneyu anamlasa mutu, namchitira zomchititsa manyazi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Munthu uja adatumanso wantchito wina, koma alimi aja adamtema m'mutu nkumunyazitsa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Kenaka anatumizanso wantchito wina kwa iwo. Iwo anamumenya munthuyo pamutu ndipo anamuzunza mochititsa manyazi.

Onani mutuwo Koperani




Marko 12:4
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Hanuni anatenga anyamata a Davide, nawameta, nadula malaya ao pakati kufikira m'matako, nawaleka achoke.


Indedi Mulungu adzaphwanya mutu wa adani ake, pakati pamutu pa iye woyendabe m'kutsutsika kwake.


Ndipo iwo anamtenga iye, nampanda, namchotsa wopanda kanthu.


Ndipo anatuma wina; iyeyu anamupha; ndi ena ambiri; ena anawapanda, ndi ena anawapha.


Ndipo anatumizanso kapolo wina; ndipo iyenso anampanda, namchitira chipongwe, nambweza, wopanda kanthu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa