Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 12:21 - Buku Lopatulika

21 ndipo wachiwiri anamkwatira, nafa, wosasiya mbeu; ndipo wachitatunso anatero momwemo;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 ndipo wachiwiri anamkwatira, nafa, wosasiya mbeu; ndipo wachitatunso anatero momwemo;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 Wachiŵiri adamtenga mai uja, nayenso nkumwalira osasiya mwana. Wachitatunso chimodzimodzi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Wachiwiri anakwatira mkazi wamasiyeyo, koma iye anamwalira wosabereka mwana. Zinali chimodzimodzi ndi wachitatu.

Onani mutuwo Koperani




Marko 12:21
2 Mawu Ofanana  

Analipo abale asanu ndi awiri; woyamba anakwatira mkazi, nafa, wosasiya mbeu;


ndipo asanu ndi awiriwo analibe kusiya mbeu. Potsiriza pake pa onse mkazinso anafa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa