Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 12:22 - Buku Lopatulika

22 ndipo asanu ndi awiriwo analibe kusiya mbeu. Potsiriza pake pa onse mkazinso anafa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 ndipo asanu ndi awiriwo analibe kusiya mbeu. Potsiriza pake pa onse mkazinso anafa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Mpaka asanu ndi aŵiri onse aja adamwalira osasiya mwana. Potsiriza pake mai uja nayenso adamwalira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Kunena zoona, palibe ndi mmodzi yemwe wa asanu ndi awiriwo anasiya ana. Pomaliza, mkaziyo anamwaliranso.

Onani mutuwo Koperani




Marko 12:22
2 Mawu Ofanana  

ndipo wachiwiri anamkwatira, nafa, wosasiya mbeu; ndipo wachitatunso anatero momwemo;


Pakuuka adzakhala mkazi wa yani wa iwowa? Pakuti asanu ndi awiriwo adamuyesa mkazi wao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa