Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Marko 12:20 - Buku Lopatulika

20 Analipo abale asanu ndi awiri; woyamba anakwatira mkazi, nafa, wosasiya mbeu;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Analipo abale asanu ndi awiri; woyamba anakwatira mkazi, nafa, wosasiya mbeu;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Tsono padaali anthu asanu ndi aŵiri pachibale pao. Woyamba adaakwatira mkazi, namwalira opanda mwana.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Tsopano panali abale asanu ndi awiri. Woyamba anakwatira namwalira wosabereka ana.

Onani mutuwo Koperani




Marko 12:20
4 Mawu Ofanana  

Mphunzitsi, Mose anatilembera, kuti, Akafa mbale wake wa munthu, nasiya mkazi, wosasiya mwana, mbale wake atenge mkazi wake, namuukitsire mbale wakeyo mbeu.


ndipo wachiwiri anamkwatira, nafa, wosasiya mbeu; ndipo wachitatunso anatero momwemo;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa