Marko 11:8 - Buku Lopatulika8 Ndimo ambiri anayala zovala zao panjira; ndi ena zitsamba, anazidula m'minda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndimo ambiri anayala zovala zao panjira; ndi ena zitsamba, anazidula m'minda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Anthu ambiri ankayala zovala zao mu mseu, ena nkumayalika nthambi zamasamba zomwe ankakazithyola ku thengo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Anthu ambiri anayala mikanjo yawo pa msewu, pamene ena anayala nthambi zomwe anadula mʼminda. Onani mutuwo |