Marko 11:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo anabwera naye mwana wa bulu kwa Yesu, naika zovala zao pa iye, ndipo Iye anakhala pamenepo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo anabwera naye mwana wa bulu kwa Yesu, naika zovala zao pa iye, ndipo Iye anakhala pamenepo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Ophunzira aja adabwera naye mwanawabuluyo kwa Yesu. Adayala zovala zao pamsana pa bulu uja, Yesu nkukwerapo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Atafika naye mwana wabulu kwa Yesu, nayika mikanjo yawo pa buluyo, Iye anakwerapo. Onani mutuwo |