Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 11:6 - Buku Lopatulika

6 Ndipo anati kwa iwo monga momwe ananena Yesu: ndipo anawalola iwo apite naye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Ndipo anati kwa iwo monga momwe ananena Yesu: ndipo anawalola iwo apite naye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Ophunzirawo adaŵayankha monga momwe adaaŵauzira Yesu. Tsono anthuwo adaŵalola kuti ammasule.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Iwo anayankha monga mmene Yesu anawawuzira, ndipo anthu aja anawalola kuti apite.

Onani mutuwo Koperani




Marko 11:6
2 Mawu Ofanana  

Ndipo ena akuima kumeneko ananena nao, Muchita chiyani ndi kumasula mwana wa bulu?


Ndipo anabwera naye mwana wa bulu kwa Yesu, naika zovala zao pa iye, ndipo Iye anakhala pamenepo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa