Marko 11:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo ena akuima kumeneko ananena nao, Muchita chiyani ndi kumasula mwana wa bulu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo ena akuima kumeneko ananena nao, Muchita chiyani ndi kumasula mwana wa bulu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Anthu amene adaali pamenepo adaŵafunsa kuti, “Inu nchiyani chimenecho, buluyo mukummasuliranji?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 anthu ena amene anayima pomwepo anafunsa kuti, “Mukuchita chiyani, kumasula mwana wabuluyo?” Onani mutuwo |