Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 11:4 - Buku Lopatulika

4 Ndipo anachoka, napeza mwana wa bulu womangidwa pakhomo, pabwalo m'khwalala, nammasula iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ndipo anachoka, napeza mwana wa bulu womangidwa pakhomo, pabwalo m'khwalala, nammasula iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Ophunzira aja adapitadi, nakapeza mwanawabuluyo ali chimangirire pa khomo m'mbali mwa mseu, ndipo adayamba kummasula.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Anapita ndipo anakapeza mwana wabulu ali kunja mu msewu waukulu atamumangirira pa chipata. Pamene anamumasula,

Onani mutuwo Koperani




Marko 11:4
8 Mawu Ofanana  

nanena kwa iwo, Mukani kumudzi wopenyana ndi inu, ndipo pomwepo mudzapeza bulu womangidwa, ndi mwana wake pamodzi naye, masulani iwo, mudze nao kwa Ine.


Ndipo ophunzira anachita monga Yesu anawauza, nakonza Paska.


Ndipo munthu akati kwa inu, Mutero bwanji? Katini, Ambuye amfuna iye; ndipo pomwepo adzamtumiza kuno.


Ndipo ena akuima kumeneko ananena nao, Muchita chiyani ndi kumasula mwana wa bulu?


Amake ananena kwa atumiki, Chimene chilichonse akanena kwa inu, chitani.


Ndi chikhulupiriro Abrahamu, poitanidwa, anamvera kutuluka kunka kumalo amene adzalandira ngati cholowa; ndipo anatuluka wosadziwa kumene akamukako.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa