Marko 11:21 - Buku Lopatulika21 Ndipo Petro anakumbukira, nanena naye, Rabi, onani, wafota mkuyuwo munautemberera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ndipo Petro anakumbukira, nanena naye, Rabi, onani, wafota mkuyuwo munautemberera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Apo Petro adakumbuka zijazi, ndipo adauza Yesu kuti, “Aphunzitsi, taonani, mkuyu uja mudautembererawu wauma.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Petro anakumbukira nati kwa Yesu, “Aphunzitsi, taonani! Mtengo wamkuyu munawutemberera uja wafota!” Onani mutuwo |