Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 11:22 - Buku Lopatulika

22 Ndipo Yesu anayankha nanena nao, Khulupirirani Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Ndipo Yesu anayankha nanena nao, Khulupirirani Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Yesu adaŵayankha kuti, “Muzikhala ndi chikhulupiriro mwa Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Yesu anayankha kuti, “Khalani ndi chikhulupiriro mwa Mulungu.

Onani mutuwo Koperani




Marko 11:22
10 Mawu Ofanana  

Nalawira mamawa, natuluka kunka kuchipululu cha Tekowa; ndipo potuluka iwo, Yehosafati anakhala chilili, nati, Mundimvere ine, Ayuda inu, ndi inu okhala mu Yerusalemu, limbikani mwa Yehova Mulungu wanu, ndipo mudzakhazikika; khulupirirani aneneri ake, ndipo mudzalemerera.


Khulupirirani pa Iye nyengo zonse, anthu inu, tsanulirani mitima yanu pamaso pake. Mulungu ndiye pothawirapo ife.


ndipo mutu wa Efuremu ndi Samariya, ndi mutu wa Samariya ndi mwana wa Remaliya, mukapanda kukhulupirira ndithu simudzakhazikika.


Ndipo Iye anati, Idza. Ndipo Petro anatsika m'ngalawa, nayenda pamadzi, kufika kwa Yesu.


Ndipo Iye ananena kwa iwo, Chifukwa chikhulupiriro chanu nchaching'ono: pakuti indetu ndinena kwa inu, Mukakhala nacho chikhulupiriro monga kambeu kampiru, mudzati ndi phiri ili, Senderapo umuke kuja; ndipo lidzasendera; ndipo palibe kanthu kadzakukanikani.


Ndipo Yesu anayankha, nati kwa iwo, Indedi ndinena kwa inu, Ngati mukhala nacho chikhulupiriro, osakayikakayika, mudzachita si ichi cha pa mkuyu chokha, koma ngati mudzati ngakhale kuphiri ili, Tanyamulidwa, nuponyedwe m'nyanja, chidzachitidwa.


Ndipo Yesu ananena naye, Ngati mukhoza! Zinthu zonse zitheka ndi iye wakukhulupirira.


Mtima wanu usavutike; mukhulupirira Mulungu, khulupirirani Inenso.


popeza munaikidwa m'manda pamodzi ndi Iye muubatizo, momwemonso munaukitsidwa pamodzi ndi Iye m'chikhulupiriro cha machitidwe a Mulungu, amene anamuukitsa Iye kwa akufa.


Paulo, kapolo wa Mulungu, ndi mtumwi wa Yesu Khristu, monga mwa chikhulupiriro cha osankhika a Mulungu, ndi chizindikiritso cha choonadi chili monga mwa chipembedzo,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa