Marko 11:20 - Buku Lopatulika20 Ndipo m'mene anapitapo m'mawa mwake, anaona kuti mkuyu uja unafota, kuyambira kumizu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ndipo m'mene anapitapo m'mawa mwake, anaona kuti mkuyu uja unafota, kuyambira kumizu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 M'maŵa mwake, m'mamaŵa ndithu, iwo akuyenda mu mseu, adaona mkuyu uja waumiratu wonse ndi mizu yomwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Mmamawa, pamene ankayenda, anaona mtengo wamkuyu uja utafota kuyambira ku mizu. Onani mutuwo |