Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 10:9 - Buku Lopatulika

9 Chifukwa chake chimene Mulungu anachimanga pamodzi, asachilekanitse munthu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Chifukwa chake chimene Mulungu anachimanga pamodzi, asachilekanitse munthu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Tsono zimene Mulungu wazilumikiza pamodzi, munthu asazilekanitse.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Chifukwa chake chimene Mulungu wachilumikiza pamodzi, munthu wina asachilekanitse.”

Onani mutuwo Koperani




Marko 10:9
4 Mawu Ofanana  

Ndipo m'nyumba ophunzira anamfunsanso za chinthu ichi.


ndipo awiriwa adzakhala thupi limodzi: kotero kuti salinso awiri, koma thupi limodzi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa