Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 10:10 - Buku Lopatulika

10 Ndipo m'nyumba ophunzira anamfunsanso za chinthu ichi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Ndipo m'nyumba ophunzira anamfunsanso za chinthu ichi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Pamene adaloŵanso m'nyumba, ophunzira adamufunsanso Yesu za nkhani yomweyi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Pamene analinso mʼnyumba, ophunzira anamufunsa Yesu za izi.

Onani mutuwo Koperani




Marko 10:10
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Iye ananena nao, Munthu aliyense akachotsa mkazi wake, nakakwatira wina, achita chigololo kulakwira mkaziyo;


Chifukwa chake chimene Mulungu anachimanga pamodzi, asachilekanitse munthu.


Ndipo pamene anakhala pa yekha, iwo amene anali pafupi ndi Iye pamodzi ndi khumi ndi awiriwo anamfunsa za mafanizo.


Ndipo pamene Iye adalowa m'nyumba, ophunzira ake anamfunsa m'tseri, kuti, Nanga bwanji sitinathe ife kuutulutsa?


Ndipo iwo anadza ku Kapernao; ndipo pamene anakhala m'nyumba, Iye anawafunsa, Munalikutsutsana ninji panjira?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa