Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 10:7 - Buku Lopatulika

7 Chifukwa chake mwamuna adzasiya atate wake ndi amai wake, ndipo adzaphatikizana ndi mkazi wake;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Chifukwa chake mwamuna adzasiya atate wake ndi amai wake, ndipo adzaphatikizana ndi mkazi wake;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Nchifukwa chake mwamuna azisiya atate ndi amai, nakaphatikizana ndi mkazi wake,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 ‘Pa chifukwa ichi mwamuna adzasiya abambo ake ndi amayi ake nakaphatikana ndi mkazi wake,

Onani mutuwo Koperani




Marko 10:7
3 Mawu Ofanana  

Chifukwa chotero mwamuna adzasiya atate wake ndi amake nadzadziphatika kwa mkazi wake: ndipo adzakhala thupi limodzi.


Chifukwa cha ichi munthu azisiya atate ndi amai, nadzaphatikizana ndi mkazi wake; ndipo iwo awiri adzakhala thupi limodzi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa