Marko 10:6 - Buku Lopatulika6 Koma kuyambira pa chiyambi cha malengedwe anawapanga mwamuna ndi mkazi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Koma kuyambira pa chiyambi cha malengedwe anawapanga mwamuna ndi mkazi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Komatu pachiyambi paja, pamene Mulungu adalenga zonse, adaŵalenga anthu, wina wamwamuna wina wamkazi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Koma pachiyambi cha chilengedwe, Mulungu ‘analenga iwo, mwamuna ndi mkazi.’ Onani mutuwo |