Marko 10:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo anati, Mose analola kulembera kalata yachilekaniro, ndi kumchotsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo anati, Mose analola kulembera kalata wakulekanira, ndi kumchotsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Iwo adati, “Mose adalola kuti munthu azilembera mkazi wake kalata yachisudzulo kenaka nkumuchotsa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Iwo anati, “Mose amaloleza mwamuna kulemba kalata ya chisudzulo ndi kumuchotsa mkazi.” Onani mutuwo |