Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 10:3 - Buku Lopatulika

3 Ndipo Iye anayankha nati kwa iwo, Kodi Mose anakulamulani chiyani?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Ndipo Iye anayankha nati kwa iwo, Kodi Mose anakulamulani chiyani?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Koma Yesu poyankha adati, “Kodi Mose adakulamulani zotani?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Iye anayankha kuti, “Kodi Mose anakulamulani chiyani?”

Onani mutuwo Koperani




Marko 10:3
6 Mawu Ofanana  

Kuchilamulo ndi kuumboni! Ngati iwo sanena malinga ndi mau awa, ndithu sadzaona mbandakucha.


Ndipo anadza kwa Iye Afarisi, namfunsa Iye ngati kuloledwa kuti munthu achotse mkazi wake, namuyesa Iye.


Ndipo anati, Mose analola kulembera kalata yachilekaniro, ndi kumchotsa.


Ndipo taonani, wachilamulo wina anaimirira namuyesa Iye, nanena, Mphunzitsi, ndidzalowa moyo wosatha ndi kuchita chiyani?


Musanthula m'malembo, popeza muyesa kuti momwemo muli nao moyo wosatha; ndipo akundichitira Ine umboni ndi iwo omwewo;


Ndiuzeni, inu akufuna kukhala omvera lamulo, kodi simukumva chilamulo?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa