Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Marko 10:12 - Buku Lopatulika

12 ndipo ngati mkazi akachotsa mwamuna wake, nakwatiwa ndi wina, achita chigololo iyeyu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 ndipo ngati mkazi akachotsa mwamuna wake, nakwatiwa ndi wina, achita chigololo iyeyu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Chimodzimodzinso ngati mkazi asudzula mwamuna wake, kenaka nkukwatiwa ndi wina, nayenso akuchita chigololo.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Ndipo akasiya mwamuna wake ndi kukakwatiwa ndi wina, achita chigololo.”

Onani mutuwo Koperani




Marko 10:12
3 Mawu Ofanana  

koma Ine ndinena kwa inu, kuti yense wakuchotsa mkazi wake, kosati chifukwa cha chigololo, amchititsa chigololo: ndipo amene adzakwata wochotsedwayo achita chigololo.


komanso ngati amsiya akhale osakwatiwa, kapena ayanjanitsidwenso ndi mwamunayo, ndipo mwamuna asalekane naye mkazi.


Ndipo mkazi amene ali naye mwamuna wosakhulupirira, navomera mtima iye kukhala naye pamodzi, asalekane naye mwamunayo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa