Marko 1:8 - Buku Lopatulika8 Ndakubatizani inu ndi madzi; koma Iye adzakubatizani ndi Mzimu Woyera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndakubatizani inu ndi madzi; koma Iye adzakubatizani ndi Mzimu Woyera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Ine ndakubatizani ndi madzi, koma Iyeyo adzakubatizani mwa Mzimu Woyera.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Ine ndikubatizani ndi madzi, koma Iye adzakubatizani ndi Mzimu Woyera.” Onani mutuwo |