Marko 1:40 - Buku Lopatulika40 Ndipo anadza kwa Iye wodwala khate, nampempha Iye, namgwadira, ndi kunena ndi Iye, Ngati mufuna mukhoza kundikonza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 Ndipo anadza kwa Iye wodwala khate, nampempha Iye, namgwadira, ndi kunena ndi Iye, Ngati mufuna mukhoza kundikonza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 Munthu wina wakhate adadza kwa Yesu. Adamugwadira nayamba kumdandaulira. Adati, “Mutafuna, mungathe kundichiritsa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 Munthu wakhate anabwera kwa Iye, nagwada, namupempha kuti, “Ngati mukufuna, mukhoza kundiyeretsa.” Onani mutuwo |