Marko 1:41 - Buku Lopatulika41 Ndipo Yesu anagwidwa chifundo, natansa dzanja namkhudza iye, nanena naye, Ndifuna; khala wokonzedwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201441 Ndipo Yesu anagwidwa chifundo, natansa dzanja namkhudza iye, nanena naye, Ndifuna; khala wokonzedwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa41 Yesu adamumvera chifundo. Adatambalitsa dzanja nkumukhudza nati, “Chabwino, ndikufuna, chira!” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero41 Yesu pomva naye chifundo, anatambasula dzanja lake namukhudza munthuyo nati, “Ndikufuna, yeretsedwa!” Onani mutuwo |