Marko 1:30 - Buku Lopatulika30 Ndipo mpongozi wake wa Simoni anali gone wodwala malungo; ndipo pomwepo anamuuza za iye: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Ndipo mpongozi wake wa Simoni anali gone wodwala malungo; ndipo pomwepo anamuuza za iye: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Apongozi a Simoni anali gone, akudwala malungo, ndipo nthaŵi yomweyo anthu adamufotokozera za matendawo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Mpongozi wa Simoni anali chigonere akudwala malungo, ndipo anamuwuza Yesu za iye. Onani mutuwo |