Maliro 5:3 - Buku Lopatulika3 Ndife amasiye opanda atate, amai athu akunga akazi amasiye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndife amasiye opanda atate, amai athu akunga akazi amasiye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Ife tili ngati ana amasiye, opanda bambo wao. Amai athu ali ngati akazi amasiye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Takhala amasiye ndi wopanda abambo, amayi athu ali ngati akazi amasiye. Onani mutuwo |