Maliro 5:2 - Buku Lopatulika2 Cholowa chathu chasanduka cha alendo, ndi nyumba zathu za achilendo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Cholowa chathu chasanduka cha alendo, ndi nyumba zathu za achilendo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Choloŵa chathu chaperekedwa kwa alendo, nyumba zathu zili m'manja mwa anthu akudza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Apereka cholowa chathu kwa obwera, nyumba zathu kwa alendo. Onani mutuwo |