Maliro 5:1 - Buku Lopatulika1 Yehova, kumbukirani chotigwerachi, penyani nimuone chitonzo chathu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Yehova, kumbukirani chotigwerachi, penyani nimuone chitonzo chathu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Inu Chauta, kumbukirani zimene zatigwera. Muyang'ane, muwone m'mene anthu akutinyozera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Inu Yehova, kumbukirani zimene zinatichitikira; yangʼanani ndipo muone kunyozeka kwathu. Onani mutuwo |