Maliro 5:4 - Buku Lopatulika4 Tinamwa madzi athu ndi ndalama, tiona nkhuni zathu pozigula. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Tinamwa madzi athu ndi ndalama, tiona nkhuni zathu pozigula. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Madzi amene timamwaŵa tiyenera kuchita chogula. Nkhuni zosonkhera moto nzoyeneranso kuchita chogula. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Tiyenera kugula madzi amene timamwa, nkhuni zathunso nʼzogula. Onani mutuwo |