Maliro 4:9 - Buku Lopatulika9 Ophedwa ndi lupanga amva bwino kupambana ophedwa ndi njala; pakuti amenewa angokwalika napyozedwa, posowa zipatso za m'munda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ophedwa ndi lupanga amva bwino kupambana ophedwa ndi njala; pakuti amenewa angokwalika napyozedwa, posowa zipatso za m'munda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Amene adaphedwa pa nkhondo anali amwai kwambiri kupambana amene adafa ndi njala. Ameneŵa ankafooka pang'onopang'ono mpaka kutsirizika, chifukwa chosoŵa chakudya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Amene anaphedwa ndi lupanga aliko bwino kuposa amene anafa ndi njala; chifukwa chosowa chakudya cha mʼmunda iwowa ankafowoka ndi njala mpaka kufa. Onani mutuwo |