Maliro 4:10 - Buku Lopatulika10 Manja a akazi achisoni anaphika ana aoao; anali chakudya chao poonongeka mwana wamkazi wa anthu a mtundu wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Manja a akazi achisoni anaphika ana aoao; anali chakudya chao poonongeka mwana wamkazi wa anthu a mtundu wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ngakhale akazi achifundo ndi manja ao omwe adafika pophika ana ao. Ana aowo adasanduka chakudya chao pa nthaŵi imene anthu anga adaonongedwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Amayi achifundo afika pophika ana awo enieni, ndiwo anali chakudya chawo pamene anthu anga anali kuwonongeka. Onani mutuwo |