Maliro 4:4 - Buku Lopatulika4 Lilime la mwana woyamwa limamatira kumalakalaka kwake ndi ludzu; ana aang'ono apempha mkate koma palibe wakuwanyemera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Lilime la mwana woyamwa limamatira kumalakalaka kwake ndi ludzu; ana ang'ono apempha mkate koma palibe wakuwanyemera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Lilime la mwana wakhanda limakangamira kukhosi chifukwa cha ludzu. Ana aang'ono amafuna chakudya, koma palibe woŵapatsa mpang'ono pomwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Lilime la mwana lakangamira kukhosi chifukwa cha ludzu, ana akupempha chakudya, koma palibe amene akuwapatsa. Onani mutuwo |