Maliro 4:3 - Buku Lopatulika3 Angakhale ankhandwe amapatsa bere, nayamwitsa ana ao; koma mwana wamkazi wa anthu a mtundu wanga wasanduka wankhanza, ngati nthiwatiwa za m'chipululu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Angakhale ankhandwe amapatsa bere, nayamwitsa ana ao; koma mwana wamkazi wa anthu a mtundu wanga wasanduka wankhanza, ngati nthiwatiwa za m'chipululu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Ngakhale nkhandwe siziwumira bere, zimayamwitsa ana. Koma anthu anga ndi ankhalwe, ali ngati nthiŵatiŵa zakunkhalango. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Ngakhale nkhandwe zimapereka bere kuyamwitsa ana ake, koma anthu anga asanduka ankhanza ngati nthiwatiwa mʼchipululu. Onani mutuwo |