Maliro 4:2 - Buku Lopatulika2 Ana a Ziyoni a mtengo wapatali, olingana ndi golide woyengetsa, angoyesedwa ngati mbiya zadothi zozipanga manja a woumba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ana a Ziyoni a mtengo wapatali, olingana ndi golide woyengetsa, angoyesedwa ngati mbiya zadothi zozipanga manja a woumba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Onani ana okondedwa a m'Ziyoni amene kale anali ngati golide kwa ife, tsopano akuŵayesa mbiya zadothi zimene woumba amachita kuumba ndi manja ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Haa! Ana a Ziyoni amtengowapatali amene kale anali ngati golide, tsopano ali ngati miphika ya dothi, ntchito ya owumba mbiya! Onani mutuwo |