Maliro 4:5 - Buku Lopatulika5 Omwe anadya zolongosoka angosiyidwa m'makwalala; omwe analeredwa navekedwa mlangali afungatira madzala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Omwe anadya zolongosoka angosiyidwa m'makwalala; omwe analeredwa navekedwa mlangali afungatira madzala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Amene ankadya zokoma akuthera m'miseu. Amene ankavala zokongola zokhazokha tsopano ali gone pa dzala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Iwo amene kale ankadya zonona akupemphetsa mʼmisewu ya mu mzinda. Iwo amene kale ankavala zokongola tsopano akugona pa phulusa. Onani mutuwo |