Maliro 2:9 - Buku Lopatulika9 Zipata zake zalowa pansi; waononga ndi kuthyola mipiringidzo yake; mfumu yake ndi akalonga ake ali pakati pa amitundu akusowa chilamulo; inde, aneneri ake samalandira masomphenya kwa Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Zipata zake zalowa pansi; waononga ndi kuthyola mipiringidzo yake; mfumu yake ndi akalonga ake ali pakati pa amitundu akusowa chilamulo; inde, aneneri ake samalandira masomphenya kwa Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Zipata za mzindawo zakwiririka pansi. Mipiringidzo yake yathyoka ndi kusakazika. Mfumu yake ndi akalonga ake ali ku ukapolo pakati pa anthu akunja, malamulo a Mulungu palibenso oŵalalika. Aneneri ake omwe sakuchitanso zija zoona zinthu m'masomphenya zochokera kwa Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Zipata za Yerusalemu zalowa pansi; wathyola ndi kuwononga mipiringidzo yake. Mfumu ndi akalonga ake agwidwa ukapolo pakati pa mitundu ya anthu, palibenso lamulo, ndipo aneneri ake sakupeza masomphenya kuchokera kwa Yehova. Onani mutuwo |