Maliro 2:10 - Buku Lopatulika10 Akulu a mwana wamkazi wa Ziyoni akhala pansi natonthola; aponya fumbi pa mitu yao, anamangirira chiguduli m'chuuno mwao: Anamwali a ku Yerusalemu aweramitsa pansi mitu yao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Akulu a mwana wamkazi wa Ziyoni akhala pansi natonthola; aponya fumbi pa mitu yao, anamangirira chiguduli m'chuuno mwao: Anamwali a ku Yerusalemu aweramitsa pansi mitu yao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Akuluakulu a mu mzinda wa Ziyoni, akhala pansi atangoti chete. Adzithira fumbi kumutu, ndipo avala ziguduli. Anamwali a ku Yerusalemu aŵeramitsa mitu yao pansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Akuluakulu a mwana wamkazi wa Ziyoni akhala chete pansi; awaza fumbi pa mitu yawo ndipo avala ziguduli. Anamwali a Yerusalemu aweramitsa mitu yawo pansi. Onani mutuwo |