Maliro 2:8 - Buku Lopatulika8 Yehova watsimikiza mtima kupasula linga la mwana wamkazi wa Ziyoni; watambalika chingwe, osabweza dzanja lake kuti lisaonongepo; waliritsa tchemba ndi linga; zilefuka pamodzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Yehova watsimikiza mtima kupasula linga la mwana wamkazi wa Ziyoni; watambalika chingwe, osabweza dzanja lake kuti lisaonongepo; waliritsa tchemba ndi linga; zilefuka pamodzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Chauta adaatsimikiza zoti aononge malinga a mzinda wa Ziyoni. Adauyesa ndi chingwe chake, ndipo sadafune kuleka kuuwononga kotheratu. Adaliritsa okhala pa malinga ndi pa makoma ake, onsewo akuzunzikira limodzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Yehova anatsimikiza kugwetsa makoma a mwana wamkazi wa Ziyoni. Anawayesa ndi chingwe ndipo sanafune kuleka kuwagwetsa. Analiritsa malinga ndi makoma; onse anawonongeka pamodzi. Onani mutuwo |