Maliro 2:3 - Buku Lopatulika3 Pokwiya moopsa walikha nyanga zonse za Israele; wabweza m'mbuyo dzanja lake lamanja pamaso pa adaniwo, natentha Yakobo ngati moto wamalawi wonyambita mozungulira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pokwiya moopsa walikha nyanga zonse za Israele; wabweza m'mbuyo dzanja lake lamanja pamaso pa adaniwo, natentha Yakobo ngati moto wamalawi wonyambita mozungulira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Chauta atapsa mtima adathyola nyonga zomwe ankanyadira Israele. Adabweza dzanja lake loteteza, adani atayandikira. Mkwiyo wake udalanga fuko la Yakobe ngati moto walaŵilaŵi wonka nuwononga zonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Atakwiya kwambiri, Ambuye anathyola nyanga iliyonse ya Israeli. Anabweza dzanja lake lamanja pamene mdani anamuyandikira. Ambuye anatentha fuko la Yakobo ngati moto wonyeketsa umene umawononga zinthu zonse zomwe zili pafupi. Onani mutuwo |