Machitidwe a Atumwi 9:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo Saulo anauka; koma potseguka maso ake, sanapenye kanthu; ndipo anamgwira dzanja, namtenga nalowa naye mu Damasiko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo Saulo anauka; koma potseguka maso ake, sanapenya kanthu; ndipo anamgwira dzanja, namtenga nalowa naye m'Damasiko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Saulo adadzuka, koma pamene maso ake adaphenyuka, sadathe kupenya kanthu. Tsono anzake aja adamgwira pa dzanja naloŵa naye m'Damasiko. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Saulo anayimirira, ndipo pamene anatsekula maso ake sanathe kuona. Kotero anamugwira dzanja ndi kulowa naye mu Damasiko. Onani mutuwo |