Machitidwe a Atumwi 9:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo anakhala masiku atatu wosaona, ndipo sanadye kapena kumwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo anakhala masiku atatu wosaona, ndipo sanadya kapena kumwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Ndipo adakhala masiku atatu osatha kupenya ndiponso osadya kapena kumwa kanthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Anakhala wosaona kwa masiku atatu ndiponso sanadye kapena kumwa kanthu kalikonse. Onani mutuwo |