Machitidwe a Atumwi 9:5 - Buku Lopatulika5 Koma anati, Ndinu yani Mbuye? Ndipo anati, Ndine Yesu amene umlondalonda; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Koma anati, Ndinu yani Mbuye? Ndipo anati, Ndine Yesu amene umlondalonda; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Iye adafunsa kuti, “Ndinu yani, Ambuye?” Iwo adati, “Ndine Yesu amene ukundizunza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Saulo anafunsa kuti, “Ndinu yani Ambuye?” Ambuye anayankha kuti, “Ndine Yesu amene iwe ukumuzunza.” Onani mutuwo |