Machitidwe a Atumwi 9:4 - Buku Lopatulika4 ndipo anagwa pansi, namva mau akunena naye, Saulo, Saulo, Undilondalonderanji? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 ndipo anagwa pansi, namva mau akunena naye, Saulo, Saulo, Undilondalonderanji? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Adagwa pansi namva mau akuti, “Saulo, Saulo, ukundizunziranji Ine?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Iye anagwa pansi ndipo anamva mawu akuti, “Saulo, Saulo ukundizunziranji Ine?” Onani mutuwo |