Machitidwe a Atumwi 9:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo poyenda ulendo wake, kunali kuti iye anayandikira Damasiko: ndipo mwadzidzidzi kudawala momzingira kuunika kochokera kumwamba; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo poyenda ulendo wake, kunali kuti iye anayandikira Damasiko: ndipo mwadzidzidzi kudawala momzingira kuunika kochokera kumwamba; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Ali paulendo wakewo, adayandikira mzinda wa Damasiko uja. Mwadzidzidzi kuŵala kochokera kumwamba kudamzinga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Akuyandikira ku Damasikoku paulendo wake, mwadzidzidzi kuwala kochokera kumwamba kunamuzungulira iye. Onani mutuwo |