Machitidwe a Atumwi 9:12 - Buku Lopatulika12 ndipo anaona mwamuna dzina lake Ananiya, alikulowa, namuika manja, kuti apenyenso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 ndipo anaona mwamuna dzina lake Ananiya, alikulowa, namuika manja, kuti apenyenso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 ndipo waona m'masomphenya munthu wina, dzina lake Ananiya, akuloŵa ndi kumsanjika manja kuti apenyenso.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Ndipo waona mʼmasomphenya munthu, dzina lake Hananiya atabwera ndi kumusanjika manja kuti aonenso.” Onani mutuwo |