Machitidwe a Atumwi 9:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo Ananiya anayankha nati, Ambuye, ndamva ndi ambiri za munthu uyu, kuti anachitiradi choipa oyera mtima anu mu Yerusalemu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo Ananiya anayankha nati, Ambuye, ndamva ndi ambiri za munthu uyu, kuti anachitiradi choipa oyera mtima anu m'Yerusalemu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Atamva zimenezo Ananiya adati, “Ambuye, anthu ambiri andiwuza za munthu ameneyu, kuti adaŵachita zoipa zambiri anthu anu ku Yerusalemu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Hananiya anayankha kuti, “Ambuye, ndinamva zambiri za munthu uyu ndi zonse zoyipa anachitira oyera mtima a ku Yerusalemu. Onani mutuwo |