Machitidwe a Atumwi 8:9 - Buku Lopatulika9 Koma panali munthu dzina lake Simoni amene adachita matsenga m'mzindamo kale, nadabwitsa anthu a Samariya, ndi kunena kuti iye yekha ndiye munthu wamkulu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Koma panali munthu dzina lake Simoni amene adachita matsenga m'mudzimo kale, nadabwitsa anthu a Samariya, ndi kunena kuti iye yekha ndiye munthu wamkulu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Koma mumzindamo munali munthu wina, dzina lake Simoni amene kale ankachita matsenga, namadodometsa anthu onse a ku Samariyako. Iyeyu ankadzimveketsa kuti ndi munthu wamkulu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Koma mu mzindawo munali munthu dzina lake Simoni, amene amachita za matsenga ndi kudabwitsa anthu a mu Samariya. Iye amadzitamandira kuti ndi wopambana, Onani mutuwo |