Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 7:54 - Buku Lopatulika

54 Koma pakumva izi analaswa mtima, namkukutira mano.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

54 Koma pakumva izi analaswa mtima, namkukutira mano.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

54 Pamene abwalo aja adamva mau a Stefanowo, adakwiya kwabasi, namchitira tsinya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

54 Atamva zimenezi, iwo anakwiya kwambiri ndipo anamukukutira mano.

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 7:54
13 Mawu Ofanana  

Iye ananding'amba m'kundida kwake, nakwiya nane, anandikukutira mano; mdani wanga ananditong'olera maso ake.


Woipa adzaziona, nadzapsa mtima; adzakukuta mano, nadzasungunuka; chokhumba oipa chidzatayika.


Pakati pa onyodola pamadyerero, anandikukutira mano.


Adani ako onse ayasamira pa iwe, atsonya nakukuta mano, nati, Taumeza; ndithu ili ndi tsiku tinaliyembekezalo, talipeza, taliona.


ndipo adzawataya iwo m'ng'anjo yamoto; kumeneko kudzakhala kulira ndi kukukuta mano.


nadzawataya m'ng'anjo yamoto; komweko kudzakhala kulira ndi kukukuta mano.


Pomwepo mfumu inati kwa atumiki, Mumange iye manja ndi miyendo, mumponye kumdima wakunja; komweko kudzali kulira ndi kukukuta mano.


nadzamdula, nadzaika pokhala pake ndi anthu onyenga; pomwepo padzakhala kulira ndi kukukuta mano.


Ndipo ponyani kapoloyo wopanda pake kumdima wakunja; kumene kudzakhala kulira ndi kukukuta mano.


koma anawo a Ufumu adzatayidwa kumdima wakunja; komweko kudzakhala kulira ndi kukukuta mano.


Kudzakhala komweko kulira ndi kukukuta mano, pamene mudzaona Abrahamu, ndi Isaki, ndi Yakobo, ndi aneneri onse, mu Ufumu wa Mulungu, koma inu nokha mutulutsidwa kunja.


Koma m'mene anamva iwo analaswa mtima, nafuna kuwapha.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa