Machitidwe a Atumwi 7:54 - Buku Lopatulika54 Koma pakumva izi analaswa mtima, namkukutira mano. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201454 Koma pakumva izi analaswa mtima, namkukutira mano. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa54 Pamene abwalo aja adamva mau a Stefanowo, adakwiya kwabasi, namchitira tsinya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero54 Atamva zimenezi, iwo anakwiya kwambiri ndipo anamukukutira mano. Onani mutuwo |